
Dr. Hutchens ndi m’busa yemwe anayambitsa Mpingo wa Gospel Life Baptist komanso ndi tsogoleri wa Euro-African Baptist Mission, bungweri liri ku zomba Malawi. Dr. Hutchens watumikirapo mipingo iwiri ku United States ndipo ali ndi Ph.D. mu maphunziro otchedwa Biblical Theology kuchokera ku The Southern Baptist Theological Seminary. Iye ndi mkazi wake Stacy ali ndi ana asanu.
God shows grace to his people.
We are Christians in that we are followers of Christ.
We worship God because of his greatness and the goodness of Jesus Christ.
Living by the spirit.
Remain firm in God’s promises.
The seed of a woman(through Abraham’s wife)
Jesus the true God and eternal life.
“Ndiphunzitseni njira yanu Yehova,
ndipo ndidzayenda mʼchoonadi chanu”
Salimo 86:11