Funsa Mafunso

Dr. Joshua Hutchens

Dr. Hutchens ndi m’busa yemwe anayambitsa Mpingo wa Gospel Life Baptist komanso ndi Mtsogoleri wa Euro-African Baptist Mission, bungweri liri ku zomba Malawi. Dr Hutchens watumikirapo mipingo iwiri mu mzinda wa United States ndipo ali ndi Ph.D. mu maphunziro otchedwa Biblical Theology kuchokera ku The Southern Baptist Theological Seminary. Iye ndi mkazi wake Stacy ali ndi ana asanu.

Mafunso