Kodi mukutsatira Yesu Khristu?/Are you following Jesus Christ?

Gawani

Abusa a Justin alongosola momveka bwino pogwiritsa ntchito ndime za malemba zosiyanasiaya kulimbikitsa Akhristu kuti apitilize kutsatira Yesu Khristu pa moyo wawo wa tsiku ndi tsiku. Abusawa agwiritsa ntchito mafunso osiyanasiyana omwe akufunsa onse omwe ndi Akhristu kuti kodi ife timadziwika chiyani ngati akhristu? Popeza tinayitanidwa kukhala okhulupirira ake a Yesu ndi otsatira akenso.

Pastor Justin explains very well different passages in the bible encouraging Christians to continue following Jesus Christ in their every day living. This pastor uses a series of questions to help make the point. And one of the most decorated questions is; How are we known as Christians? Are we able to stand out as true Christians? For we were called to believe and follow Jesus Christ.