Timapembedza mulungu chifukwa chiyani?/Why do we worship God?

Gawani

Genesis 14:16-24 mu chaputa cha bukuli abusa a Joshua Hutchens afunsa mafunso ophweka kumvetsa koma ovuta kuyankha. Izi achita ndi cholinga chofuna kuthandiza kumvetsetsa ndime ya malemba imeneyi. Mafunso ali motere; Ndi chifukwa chiyani timapembeza mulungu? Ndi chifukwa chiyani timapereka chuma chathu kwa mulungu? Ndi chifukwa chiyani timakhala moyo wa khristu okhulupirika? Yankho la mafunso awa lithandiza kumvetsa bwino ndime imeneyi. Uthenga omwe ukupezeka mu ndime imeneyi ndi ofanana ndi wa mu gawo loyamba la chaputa ichi. Mulungu amatipumulutsa kumachimo athu kudzera mwa mfumu yozichepetsa Yesu Khristu. Ndipo tikuonanso kuti mulungu akapanga malonjezo ake ndi iye mwini amakwaniritsa. Motero kuti timapebedza mulungu chifukwa cha ukulu wake ndi ubwino wa Yesu Khristu.

Genesis 14:16-24 in this chapter pastor Joshua Hutchens asks simple questions but hard to answer in order to help understand this passage. And the questions are as follows; Why do we worship God? Why do we give our offerings to God? Why do we live a life of a faithful Christian? The answer to these questions would help in understanding this passage. The message in this chapter is the same as that in the first part of this chapter and that is God rescues us from our sins through a humble king Jesus Christ. And we see God making his promises to Abraham and at the same time he is the one who fulfills them. Many things can be said about this passage. And finally we worship God because of his greatness and the goodness of Jesus Christ.