Chivumbulutso cha nthawi ya “msautso” m’masiku omaliza/The Revelation of the “great tribulation” in the ladder days
Chivumbulutso cha nthawi ya msautso m’masiku omaliza
Dr. Hutchens ndi m’busa yemwe anayambitsa Mpingo wa Gospel Life Baptist komanso ndi tsogoleri wa Euro-African Baptist Mission, bungweri liri ku zomba Malawi. Dr. Hutchens watumikirapo mipingo iwiri ku United States ndipo ali ndi Ph.D. mu maphunziro otchedwa Biblical Theology kuchokera ku The Southern Baptist Theological Seminary. Iye ndi mkazi wake Stacy ali ndi ana asanu.
Chivumbulutso cha nthawi ya msautso m’masiku omaliza
Jesus the lord of History and of the world
Mulungu avumbulutsa chilungamo ndi chisomo chake
Mulungu akudalitsa Kaini ndi Abele panthawi yomwe agwira ntchito zawo ndipo iwo akulandira zotsatira zabwino kuchokera ku ntchito zawozi. Panthawi yomweyo tikuona kuthokoza kosiyana komwe
Genesis 3:17-24, mu uthenga uwu tikuona chilungamo cha mulungu chikuonetsedwa chifukwa cha kusamvera kwa Adamu, komanso tikuona mulungu akupeleka chisomo kwa Adamu chifukwa cha chikhulupiriro chake.
Aroma 1:16–17. Uthenga Wabwino ndi mphamvu ya Mulungu yopulumutsa chifukwa mu Uthenga Wabwino mphatso ya Mulungu ya chilungamo ya onetsedwa.
Aroma 1:8–15. Chigonjetso cha Mwana wa Mulungu chitha kuonekera mu chikhulupiriro chathu komanso mukulalikira Uthenga Wabwino ku mayiko onse.
“Ndiphunzitseni njira yanu Yehova,
ndipo ndidzayenda mʼchoonadi chanu”
Salimo 86:11