Kukhala Wophunzira: Kukhala Moyo Wosinthika ndi Uthenga Wabwino

2 | Batizidwani

Ubatizo ndi njira yoyambirira ya kumvera monga mKhristu watsopano. Uma onetsera kwa aliyense yemwe alikunja zomwe Mulungu wachita kuti mwa munthu.

Phunzirani »

3 | Yambani Kupemphera

Kudzera mupemphero, timamva umwana wathu mubanja la Mulungu. Yesu anatiphuzitsa momwe tikuyenerera kupemphera munjira yomwe ikuyenerera ku pereka ulemerero kwa Mulungu.

Phunzirani »

8 | Kondani Anthu Ena

Dziko lidzadziwa kuti ndife ana aMulungu kudzera mu chikondi chathu. Baibulo likutilamulira ife kuti tikonde Mulungu, anasi utuu, wina ndi m’dzake, adani athu, komanso iwu omwe ndi osowa.

Phunzirani »

10 | Vulani Chikhalidwe cha Uchimo

Ana a Mulungu si a ngwiro. Amatha nthawi zina kuchimwa koma ana a Mulungu amavomereza matchimo awo ndipo amafunafuna kupha machimo awo kuchokera ku mizu po khonzanso malingaliro awo ndikuvala munthu watsopano.

Phunzirani »

11 | Pirirani Mpaka Kumapeto

Imfa ya Yesu siikutitsimikizira kupindula. Akhirisitu amavutika. Koma kuvutika kumeneku ndi kuyesedwa kwa chikhulupiliro chawo. Iwo amene amakhulupiliradi sangataye chiphulumutso chawo konse, komano chikhulupiliro choonadi chimazindikirika pamene akhalabe okhulipirika mpaka kumapeto.

Phunzirani »

Dr. Joshua Hutchens

Dr. Hutchens ndi m’busa yemwe anayambitsa Mpingo wa Gospel Life Baptist komanso ndi Mtsogoleri wa Euro-African Baptist Mission, bungweri liri ku zomba Malawi. Dr Hutchens watumikirapo mipingo iwiri mu mzinda wa United States ndipo ali ndi Ph.D. mu maphunziro otchedwa Biblical Theology kuchokera ku The Southern Baptist Theological Seminary. Iye ndi mkazi wake Stacy ali ndi ana asanu.

“Nʼchifukwa chake, ngati munthu aliyense ali mwa Khristu, ndi wolengedwa kwatsopano; zinthu zakale zapita taonani, zakhala zatsopano.”

2 Akorinto 5:17​