Mbewu ya mzimayi(mwa mkazi wa Abrahamu)/The seed of a Woman(coming through Abraham’s wife)

Gawani

Genesis 12:4-8, Mulungu akupitiriza kusunga malonjeza ake omwe anawalengeza kwa Hava atachimwira mulungu. Mulungu akuchititsa mkazi wa Abrahamu yemwe anali chumba kuti akhale ndi mwana. Ndipo kutengera dongosolo la chiyambi cha moyo wa Yesu, abale ake anayambira mwa Abrahamu. Izi zikutilimbikitsa ife monga akhristu kuti tili ndi mulungu amene amasunga malonjezo ake. Mulungu analonjeza moyo wosatha mwa Yesu Khristu ndipo amawupereka kwa onse omwe atembenuka mtima ndi kusata Yesu.

Genesis 12:4-8, God keeps his promise. When Adam sinned against God and was banished, God promised crashing the head of the serpent through the seed of a woman. When God promised Abraham a nation, he did so through a barren woman. This woman was a wife to Abraham and gave birth to a child of barren. The life of Jesus on earth tells us that his relatives came from that child. This is only encouraging us christians that we have a God who cares and keeps his promises. We are confident in his promises.