Isaac Dzimbiri
Mbusa Dzimbiri amatsogolera kapembezedwe ku Mpingo wa Gospel Life Baptist komanso amatumikira alimodzi ndi Euro-Africa Baptist Mission yomwe yiri ku Zomba Malawi. M’busa Dzimbiri watumikira mipingo ya ku Malawi komanso ya ku Zambia, ndipo ali ndi M.A. mu maphunziro a zautumiki kuchokera ku Central Africa Baptist University ndi Piedmont International University.
Zoyenera kudziwa potsuzula mkazi/what to know about divorcing your wife
Mulungu amalamulira mbiri ya anthu/God controls human history
Mphamvu ndi chisankho cha mulungu/Selection and sovereignty of God
Mulungu akonda anthu ake powapatsa mpulumutsi/God gives his people a savior out of love
Nkwabwino kukhala olimba muchikhulupiriro/It is good to remain firm in the Faith
khalani anthu okonda chilungamo/Be a people that love justice
Yesu aphunzitsa ndi ulamulilo/Jesus teaches with authority
Akhristu ndi mchere wa dziko lapansi/Christians are salt of the world
Ambuye achitira Sara zomwe adalonjeza/The lord did for Sarah what he had promised
Mulungu apulumutsa Loti/God rescues Lot