11 | Pirirani Mpaka Kumapeto

Gawani


Imfa ya Yesu siikutitsimikizira kupindula. Akhirisitu amavutika. Koma kuvutika kumeneku ndi kuyesedwa kwa chikhulupiliro chawo. Iwo amene amakhulupiliradi sangataye chiphulumutso chawo konse, komano chikhulupiliro choonadi chimazindikirika pamene akhalabe okhulipirika mpaka kumapeto.

Jesus’ death does not guarantee us prosperity. Christians suffer, but this suffering is a test of our faith. Those who truly believe can never lose their salvation, but true faith is demonstrated only by remaining faithful to the end.