8 | Kondani Anthu Ena

Gawani


Dziko lidzadziwa kuti ndife ana aMulungu kudzera mu chikondi chathu. Baibulo likutilamulira ife kuti tikonde Mulungu, anasi utuu, wina ndi m’dzake, adani athu, komanso iwu omwe ndi osowa.

The world will know we are children of God by our love. The Bible commands us to love God, neighbor, one another, enemies, and those in need.