9 | Kupembeza Limodzi ndi Banja

Gawani


Pamene Mulungu anakupangani kukhala atsopano, anayamba kupanga banja lanu kukhanso latsopano. Pangani Mulungu ku khala Mulungu wa banja lanu kudzera mukupembeza kwa banja.

When God made you new, he began to make your family new. Make God the God of your home through family worship.