2 | Batizidwani

Gawani


Ubatizo ndi njira yoyambirira ya kumvera monga mKhristu watsopano. Uma onetsera kwa aliyense yemwe alikunja zomwe Mulungu wachita kuti mwa munthu.

Baptism is your first step of obedience as a new Christian. It is the public sign of your faith. It shows to everyone outside what God has done inside.