Kupirira kwa Oyera Mtima Chikhulupiriro Chawo

Isaac Dzimbiri

Mbusa Dzimbiri amatsogolera kapembezedwe ku Mpingo wa Gospel Life Baptist komanso amatumikira alimodzi ndi Euro-Africa Baptist Mission yomwe yiri ku Zomba Malawi. M’busa Dzimbiri watumikira mipingo ya ku Malawi komanso ya ku Zambia, ndipo ali ndi M.A. mu maphunziro a zautumiki kuchokera ku Central Africa Baptist University ndi Piedmont International University.

Ulaliki

Imfa, Chiwukitso komanso Mapemphero a Yesu Khristu Tsopanolingo

Oyera mtima apirira muchikhulupiriro chawo chifukwa imfa ya Yesu yachotsa chostutsa china chilichonse komanso mlandu uliwonse otsutsana ndi sosakhidwa a Mulungu. Chiukitso cha Yesu ndi chitsimikizo cha chikhulupiriro chathu komanso mpemphero ake opemperera oyera mtima amatsimikizira kuti chikhulupiriro cho sichifowoka.

Phunzirani »

“Koma kulani mu chisomo ndi mʼchidziwitso cha Ambuye ndi Mpulumutsi wathu Yesu Khristu.”

2 Petro 3:18

M'ndandanda Opitilira