2 | Limani m’Munda

Gawani


Timakhonza munda watsopano wodzalapo mpingo kudzera mupemphero. Timamupempha Mulungu kuti akonzekeretse nthaka yoti ilandire mbewu ya uthenga wa bwino. Koma tikuyeneranso kuzikonzekeretsa tokha popanga kafukufuku wa munda, kufunafuna munthu wamtendere, ndi kupanga ndondomeko zokaphunzitsa uthenga wabwino.

We prepare a new field for church planting through prayer. We ask God to prepare the soil to receive the seed of the gospel. But we must also prepare ourselves by researching the field, seeking a person of peace, and making plans to preach the gospel.