
4 | Samalirani m’Munda
Monga munda omwe wayamba kukula, akhirisitu atsopano amafunika chisamaliro chauzimu pafupipafupi. Yesu akutilamula kuti tibatize wokhulupirira atsopano ndi kuwaphunzitsa malamulo ake.
Monga munda omwe wayamba kukula, akhirisitu atsopano amafunika chisamaliro chauzimu pafupipafupi. Yesu akutilamula kuti tibatize wokhulupirira atsopano ndi kuwaphunzitsa malamulo ake.
Kudzala kachisi wa tsopano kuchokera mubaibulo, tikuyenera kudzala munda ndi mbewu ya uthenga wa wabwino. Izi zimafunika kuti tifalitse uthenga wa bwino momveka bwino komanso kwa anthu ambiri. Pamene tifalitsa uthenga wa mulungu, Yesu akutiuza kuti tiyembekeze mayankho anayi (Marko 4:11-20).
Timakhonza munda watsopano wodzalapo mpingo kudzera mupemphero. Timamupempha Mulungu kuti akonzekeretse nthaka yoti ilandire mbewu ya uthenga wa bwino. Koma tikuyeneranso kuzikonzekeretsa tokha popanga kafukufuku wa munda, kufunafuna munthu wamtendere, ndi kupanga ndondomeko zokaphunzitsa uthenga wabwino.
Cholinga chathu ndikupanga ophunzira ndipo timapanga ophunzira polalikira uthenga wabwino ndi kudzala mipingo. Kuti tidzale mpingo timayenera kukonza munda, kudzala mmunda, kusamalira munda kenaka kukolola mmunda.
Chipangano Chakale
Genesis
Eksodo
Levitiko
Numeri
Deuteronomo
Yoswa
Oweruza
Rute
1 Samueli
2 Samueli
1 Mafumu
2 Mafumu
1 Mbiri
2 Mbiri
Ezara
Nehemiya
Estere
Yobu
Masalimo
Miyambo
Mlaliki
Nyimbo ya Solomoni
Yesaya
Yeremiya
Maliro
Ezekieli
Danieli
Hoseya
Yoweli
Amosi
Obadiya
Yona
Mika
Nahumu
Habakuku
Zafaniya
Hagai
Zekariya
Malaki
Chipangano Chatsopano
Mateyu
Marko
Luka
Yohane
Machitidwe a Atumwi
Aroma
1 Akorinto
2 Akorinto
Agalatiya
Aefeso
Afilipi
Akolose
1 Atesalonika
2 Atesalonika
1 Timoteyo
2 Timoteyo
Tito
Filemoni
Ahebri
Yakobo
1 Petro
2 Petro
1 Yohane
2 Yohane
3 Yohane
Yuda
Chivumbulutso