4 | Werenga Baibulo Dr. Joshua Hutchens May 15, 2020 Kudzera mukuwerenga Baibulo, timamva Mulungu akuyakhula nafe. Khalani ndi dogosolo lakawerenge ka Baibulo komanso yambani kuwerenga. Phunzirani »
2 | Batizidwani Dr. Joshua Hutchens May 5, 2020 Ubatizo ndi njira yoyambirira ya kumvera monga mKhristu watsopano. Uma onetsera kwa aliyense yemwe alikunja zomwe Mulungu wachita kuti mwa munthu. Phunzirani »