
1 | Minda Inayi
Cholinga chathu ndikupanga ophunzira ndipo timapanga ophunzira polalikira uthenga wabwino ndi kudzala mipingo. Kuti tidzale mpingo timayenera kukonza munda, kudzala mmunda, kusamalira munda kenaka kukolola mmunda.
Cholinga chathu ndikupanga ophunzira ndipo timapanga ophunzira polalikira uthenga wabwino ndi kudzala mipingo. Kuti tidzale mpingo timayenera kukonza munda, kudzala mmunda, kusamalira munda kenaka kukolola mmunda.
Mulungu akuyitana mKhristu wina aliyense kukhala mboni ya Yesu. Kuchitira umboni wokhudzana ndi Yesu ndi kosavunga monga kuyakhula nkhani yako ndi nkhani ya Mulungu.
Timapereka chifukwa Mulungu anatipatsa ife Mwana wake. Tikuyenera kukhala ndi dogosolo la kupereka kwathu komanso tikuyenera kupeka wokondwera.
Timasokhana pamodzi kuti tipembeze ndi cholinga choti tithandizone wina ndi nzake kukula musinkhu mwa Khristu. Tikuyenera kukhala ndi chikhalidwe chopembera ndi mpingo umodzi nthawi zonse.
Kudzera mukuwerenga Baibulo, timamva Mulungu akuyakhula nafe. Khalani ndi dogosolo lakawerenge ka Baibulo komanso yambani kuwerenga.
Kudzera mupemphero, timamva umwana wathu mubanja la Mulungu. Yesu anatiphuzitsa momwe tikuyenerera kupemphera munjira yomwe ikuyenerera ku pereka ulemerero kwa Mulungu.
Ubatizo ndi njira yoyambirira ya kumvera monga mKhristu watsopano. Uma onetsera kwa aliyense yemwe alikunja zomwe Mulungu wachita kuti mwa munthu.
Chipangano Chakale
Genesis
Eksodo
Levitiko
Numeri
Deuteronomo
Yoswa
Oweruza
Rute
1 Samueli
2 Samueli
1 Mafumu
2 Mafumu
1 Mbiri
2 Mbiri
Ezara
Nehemiya
Estere
Yobu
Masalimo
Miyambo
Mlaliki
Nyimbo ya Solomoni
Yesaya
Yeremiya
Maliro
Ezekieli
Danieli
Hoseya
Yoweli
Amosi
Obadiya
Yona
Mika
Nahumu
Habakuku
Zafaniya
Hagai
Zekariya
Malaki
Chipangano Chatsopano
Mateyu
Marko
Luka
Yohane
Machitidwe a Atumwi
Aroma
1 Akorinto
2 Akorinto
Agalatiya
Aefeso
Afilipi
Akolose
1 Atesalonika
2 Atesalonika
1 Timoteyo
2 Timoteyo
Tito
Filemoni
Ahebri
Yakobo
1 Petro
2 Petro
1 Yohane
2 Yohane
3 Yohane
Yuda
Chivumbulutso