Pangano la mdulidwe/Covenant Circumcision

Gawani

Genesis 17:1-14 mu pangano la mdulidwe mukupezeka zinthu zingapo zomwe ndi zofunika kuzimvetsetsa. Abusa a Hutchens akufotokozera bwino lomwe za pangano limeneli. Pangano la mdulidwe ndi mbali imodzi yotsindika kuti mbewu idzabwera kuchokera kwa Abrahamu. Izi zikugwirizananso ndi kusinthidwa dzina kwa Abram kukhala Abrahamu tate wa anthu ambiri. Mdulidwewu ulingati chidzindikiro chososnyeza kuti Abrahamu ndi wa nsembe. Izi zili choncho popeza kuti wansembe ndi yemwe amalandira mdulidwe molingana ndi ntchitoyi. Mdulidwe ukulodzera kufunika kochita mdulidwe mitima yanthu. Pangano la mdulidwe lomwe mulungu anachita ndi Abrahamu ndi mlozo wa ife akhrisitu kuti tiyenera kukana matupi anthu awuchimo.

Genesis 17:1-14, in the covenant circumcision are important things that needs to be understood. Pastor Hutchens takes us through these important things. Covenant circumcision is one part that acts as a sign that confirms that the seed will come through Abraham. This also agrees to the changing of Abram’s name to Abraham which means the father of many. This circumcision is also a sign showing that Abraham is a priest. Because in those days only a pastor was the one circumcised in order to serve as a priest. The covenant is also a reminder that we Christians have the need to circumcise our hearts. We need to deny our sinful bodies and put on a new heart .