Khalani ophunzira weniweni wa Yesu Khristu/Be a true disciple of Jesus Christ

Gawani

Mateyu 5:1-3 ndime zamalemba izi ndi zofunika kwambiri kuwunikirana chifukwa ndi gawo limodzi la chiphunzitso chotchuka cha Yesu. Phunziro limene likupezeka mu ndime za malembazi ndi lakuti uthakukhala Nkhristu koma osakhala Nkhristu weniweni. Nkhani siyongopezeka ku malo opembedzera mulungu tsiku la mulungu kapena loweruka koma makamaka kukhala otsatira kapena ophunzira weniweni wa Yesu ngakhale masiku ena onse. Tiyenera kukhala anthu amene tapereka moyo wanthu wonse kwa Yesu , osati maola awiri okha tsiku la sabata lokha ayi koma mphindi iliyonse ya moyo.

Matthew 5:1-3 These passages are important to discuss them because they are part of the famous teachings of Jesus Christ called the sermon on the mountain. And part of the lessons of this teaching tells us that you can be a Christian but really not being a Christian. It isn’t just about being present at church every Sunday or Saturday and committing your two hour time but it’s really about being a true follower of Jesus. It means every minute of your life is committed to being a disciple of Jesus Christ.