Malankhulidwe a Pemphero/The language of Prayer

Gawani

Masalimo 5:1-12, Abusa a Dallas Goebel afokozera bwino za malankhulidwe a pemphero. Abusa a Dallas alongosora pogwiritsa ntchito Buku la Masalimo chaputa 5. Kufotokoza mwachidule, mayankhulidwe a pemphero ayenera kukhala motere; Pemphero liyenera kukhala ndi cholinga, pemphero liyenera kudzindikira kuti mulungu ndi olungama ndipo amalanga anthu omwe ndi ochimwa, pemphero liyenera kukamba za matemberero omwe amabwera chifukwa chamachimo, ndipo pempherero liyenera kuyankhula ndi kulengeza za madalitso a mulungu pa anthu ake olungama. Nkhrisitu ayenera kulingalira pemphero lake asanalipereke kwa mulungu. Ndipo ayenera kulingalira mogwirizana ndi malemba.

Psalm 5:1-12, Pastor Dallas Goebel teaches about the language of prayer. Pastor Dallas explains this from the book of Psalm chapter 5. In brief, a prayer should have the following; Prayer should be deliberate and intentional, prayer should recognize that God is righteous and he punishes sin along with those who do it, prayer should recognize the curses which come because of sin, and prayer should declare and recognize blessings of God upon those who love and fear him. A Christian should think about his/her prayer before offering it before God. And he/she should think about this biblically.