kukhala ndi njala yofuna chilungamo /Growing thirsty for righteousness

Gawani

Mateyu 5:6, funso lomveka bwino nali, kodi mumamva ludzu ndi chani? Mukapeza chomwe chapangitsa inu kumva ludzu, ludzulo limatha? Buku la Mateyu 5 ndime ya 6, tikuudzidwa za ludzu lofuna Khristu. Ludzu lofuna chilungamo. Kodi mukumasaka kuti mukhutitsidwe ndi chilungamo? Popeza Yesu akunena kuti, odala ndi omwe amva ludzu la chilungamo popeza adzakhutitsidwa. M’mipingo mwathu tikuyenera kukhala anthu omva ludzu la chilungamo chifukwa ambuye wathu Yesu akukulonjeza kuti tidzakhutitsidwa.

Matthew 5:6, here is a simple question, what makes you thirsty? And after getting what you thirsted for, are you ever quenched of the thirst? In book of Matthew 5 verse 6, we’re told of the thirst for Christ. The thirst for righteousness? Are you seeking to be filled with righteousness? For Jesus says “happy are those thirsting and hungering for righteousness for they will be filled.” In our churches we should be thirsting and hungering for righteousness and Jesus tells us that we will be filled.