
8 | Kondani Anthu Ena
Dziko lidzadziwa kuti ndife ana aMulungu kudzera mu chikondi chathu. Baibulo likutilamulira ife kuti tikonde Mulungu, anasi utuu, wina ndi m’dzake, adani athu, komanso iwu omwe ndi osowa.
Dziko lidzadziwa kuti ndife ana aMulungu kudzera mu chikondi chathu. Baibulo likutilamulira ife kuti tikonde Mulungu, anasi utuu, wina ndi m’dzake, adani athu, komanso iwu omwe ndi osowa.
Oyera mtima apirira muchikhulupiriro chawo chifukwa imfa ya Yesu yachotsa chostutsa china chilichonse komanso mlandu uliwonse otsutsana ndi sosakhidwa a Mulungu. Chiukitso cha Yesu ndi chitsimikizo cha chikhulupiriro chathu komanso mpemphero ake opemperera oyera mtima amatsimikizira kuti chikhulupiriro cho sichifowoka.
Chifukwa cha mphamvu za Mulungu ndi chifuniro chake, anthu woyera mtima apirira mu chikulupirira chawo mpaka kumapeto kwa moyo.
2 Timoteyo 1:9. Kupirira kwa anthu wokhulupirira kwa khazikika mu chikondi chosatha cha Mulungu, yemwe anatipatiratu chisomo chake mwa Yesu Khristu kutiwombola ife ku machimo athu.
Aefeso 1:4–7; Aroma 8:29–30. Chipulumutso ya oyera mtima china yamba ndi Mulungu, ndipo chidzamulizidwa ndi Mulungu. Chifukwa choti Mulungu amatsiriza ndogosolo lomwe wa liyamba adzatsirizanso dogosolo la chipulumutso cha oyera mtima.
Chipangano Chakale
Genesis
Eksodo
Levitiko
Numeri
Deuteronomo
Yoswa
Oweruza
Rute
1 Samueli
2 Samueli
1 Mafumu
2 Mafumu
1 Mbiri
2 Mbiri
Ezara
Nehemiya
Estere
Yobu
Masalimo
Miyambo
Mlaliki
Nyimbo ya Solomoni
Yesaya
Yeremiya
Maliro
Ezekieli
Danieli
Hoseya
Yoweli
Amosi
Obadiya
Yona
Mika
Nahumu
Habakuku
Zafaniya
Hagai
Zekariya
Malaki
Chipangano Chatsopano
Mateyu
Marko
Luka
Yohane
Machitidwe a Atumwi
Aroma
1 Akorinto
2 Akorinto
Agalatiya
Aefeso
Afilipi
Akolose
1 Atesalonika
2 Atesalonika
1 Timoteyo
2 Timoteyo
Tito
Filemoni
Ahebri
Yakobo
1 Petro
2 Petro
1 Yohane
2 Yohane
3 Yohane
Yuda
Chivumbulutso